Mateyu 18:31 - Buku Lopatulika31 Chifukwa chake m'mene akapolo anzake anaona zochitidwazo, anagwidwa chisoni chachikulu, nadza, nalongosolera mbuye wao zonse zimene zinachitidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Chifukwa chake m'mene akapolo anzake anaona zochitidwazo, anagwidwa chisoni chachikulu, nadza, nalongosolera mbuye wao zonse zimene zinachitidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 “Antchito anzake ena ataona zimenezi, adamva chisoni kwambiri. Adapita kukafotokozera mbuye wao zonsezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Pamene antchito ena anaona zomwe zinachitikazo, anamva chisoni kwambiri ndipo anapita nakawuza bwana wawo zonse zimene zinachitika. Onani mutuwo |