Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 18:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo iye sanafune; koma anamuka, namponya iye m'nyumba yandende, kufikira abwezere ngongole.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo iye sanafune; koma anamuka, namponya iye m'nyumba yandende, kufikira abwezere ngongole.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Koma iye adakana, nakamponyetsa m'ndende kuti mpaka abweze ndithu ngongoleyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 “Koma iye anakana. Mʼmalo mwake, anachoka nakamumangitsa kufikira atabweza ngongoleyo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 18:30
5 Mawu Ofanana  

ndipo muziti, Itero mfumu, Khazikani uyu m'kaidi, mumdyetse chakudya cha nsautso, ndi madzi a nsautso, mpaka ndikabwera ndi mtendere.


Wotseka makutu ake polira waumphawi, nayenso adzalira koma osamvedwa.


Pamenepo kapolo mnzakeyu anagwada pansi, nampempha iye, nati, Bakandiyembekeza ine, ndipo ndidzakubwezera.


Chifukwa chake m'mene akapolo anzake anaona zochitidwazo, anagwidwa chisoni chachikulu, nadza, nalongosolera mbuye wao zonse zimene zinachitidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa