Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 18:26 - Buku Lopatulika

26 Chifukwa chake kapoloyo anagwada pansi, nampembedzera, nati, Mbuye, bakandiyembekezani ine, ndipo zonse ndidzazibwezera kwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Chifukwa chake kapoloyo anagwada pansi, nampembedzera, nati, Mbuye, bakandiyembekezani ine, ndipo zonse ndidzazibwezera kwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Apo wantchito uja adamgwadira nati, ‘Pepani, ndakupembani, lezereni mtima, ndidzakubwezerani ndithu zonse.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 “Wantchitoyo anagwada pamaso pake namupempha iye kuti, ‘Lezereni mtima ndipo ndidzabweza zonse.’

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 18:26
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo kapolo mnzakeyu anagwada pansi, nampempha iye, nati, Bakandiyembekeza ine, ndipo ndidzakubwezera.


Ndipo pofika kunyumba anaona kamwanako ndi Maria amake, ndipo anagwa pansi namgwadira Iye; namasula chuma chao, nampatsa Iye mitulo, ndiyo golide ndi lubani ndi mure.


Ndipo onani, wakhate anadza namgwadira Iye, nanena, Ambuye ngati mufuna mungathe kundikonza.


Simoni anayankha, nati, Ndiyesa kuti, iye amene anamkhululukira zoposa.


Pakuti pakusadziwa chilungamo cha Mulungu, ndipo pofuna kukhazikitsa chilungamo cha iwo okha, iwo sanagonje ku chilungamo cha Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa