Mateyu 18:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo pamene anayamba kuwerengera, anadza kwa iye ndi wina wamangawa wa ndalama za matalente zikwi khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo pamene anayamba kuwerengera, anadza kwa iye ndi wina wamangawa wa ndalama za matalente zikwi khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Atangoyamba kumene, adabwera ndi wantchito wina amene anali ndi ngongole ya ndalama zochuluka kwabasi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Atangoyamba kulandira, anamubweretsa munthu kwa iye amene anakongola ndalama 10,000. Onani mutuwo |