Mateyu 18:20 - Buku Lopatulika20 Pakuti kumene kuli awiri kapena atatu asonkhanira m'dzina langa, ndili komweko pakati pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Pakuti kumene kuli awiri kapena atatu asonkhanira m'dzina langa, ndili komweko pakati pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Pajatu pamene aŵiri kapena atatu asonkhana m'dzina langa, Ineyo ndili nao pomwepo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Pakuti pamene awiri kapena atatu asonkhana pamodzi mʼdzina langa, Ine ndili nawo pomwepo.” Onani mutuwo |