Mateyu 18:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ngati mbale wako akuchimwira iwe, pita, numlangize pa nokha iwe ndi iye; ngati akumvera iwe, wambweza mbale wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ngati mbale wako akuchimwira iwe, pita, numlangize pa nokha iwe ndi iye; ngati akumvera iwe, wambweza mbale wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Mbale wako akakuchimwira, pita ukamdzudzule muli aŵiri nokha. Akakumvera, wamkonza mbale wakoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Ngati mʼbale wako akuchimwira, pita kamuwuze cholakwa chake pa awiri. Ngati akumvera, wamubweza mʼbale wakoyo. Onani mutuwo |