Mateyu 18:14 - Buku Lopatulika14 Chomwecho sichili chifuniro cha Atate wanu wa Kumwamba kuti mmodzi wa ang'ono awa atayike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chomwecho sichili chifuniro cha Atate wanu wa Kumwamba kuti mmodzi wa ang'ono awa atayike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Chonchonso Atate anu amene ali Kumwamba safuna kuti ndi mmodzi yemwe mwa anaŵa atayike. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Chimodzimodzinso Atate anu akumwamba safuna kuti mmodzi wa anawa atayike. Onani mutuwo |