Mateyu 17:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo m'mene anali kutsotsa mu Galileya, Yesu ananena nao, Mwana wa Munthu adzaperekedwa m'manja a anthu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo m'mene anali kutsotsa m'Galileya, Yesu ananena nao, Mwana wa Munthu adzaperekedwa m'manja a anthu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsiku lina ophunzira atasonkhana onse ku Galileya, Yesu adaŵauza kuti, “Mwana wa Munthu akudzaperekedwa kwa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Atasonkhana pamodzi ku Galileya, Iye anawawuza kuti, “Mwana wa Munthu akupita kukaperekedwa mʼmanja mwa anthu. Onani mutuwo |