Mateyu 16:26 - Buku Lopatulika26 Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Nanga ndiye kuti munthu angapindulenji atapata zonse zapansipano, iyeyo nkutaya moyo wake? Munthu angalipire chiyani choti aombolere moyo wake? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Kodi munthu adzapindula chiyani ngati atapeza zonse za dziko lapansi nataya moyo wake? Kapena munthu angapereke chiyani chosinthana ndi moyo wake? Onani mutuwo |