Mateyu 16:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Simoni Petro anayankha nati, Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Simoni Petro anayankha nati, Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Simoni Petro adayankha kuti, “Inu ndinu Mpulumutsi wolonjezedwa uja, Mwana wa Mulungu wamoyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Simoni Petro anayankha kuti, “Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo.” Onani mutuwo |