Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Muli nayo mikate ingati? Ndipo iwo anati, Isanu ndi iwiri, ndi tinsomba pang'ono.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Muli nayo mikate ingati? Ndipo iwo anati, Isanu ndi iwiri, ndi tinsomba pang'ono.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Yesu adaŵafunsa kuti, “Kaya buledi muli naye mngati?” Iwo aja adati, “Msanu ndi muŵiri, ndiponso tinsomba toŵerengeka.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Yesu anawafunsa kuti, “Muli ndi malofu a buledi angati?” Iwo anayankha kuti, “Asanu ndi awiri ndi tinsomba pangʼono.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:34
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira ananena kwa Iye, Tiione kuti mikate yotere m'chipululu yakukhutitsa unyinji wotere wa anthu?


Ndipo Iye analamulira anthuwo akhale pansi onse;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa