Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 15:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo Iye analamulira anthuwo akhale pansi onse;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo Iye analamulira anthuwo akhale pansi onse;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Apo Yesu adalamula anthu aja kuti akhale pansi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Iye anawuza gululo kuti likhale pansi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:35
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Muli nayo mikate ingati? Ndipo iwo anati, Isanu ndi iwiri, ndi tinsomba pang'ono.


natenga mikateyo isanu ndi iwiri ndi nsombazo; nayamika Mulungu, nanyema, napatsa kwa ophunzira, ndi ophunzira kwa anthu.


Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa