Mateyu 14:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo iye, atampangira amake, anati, Ndipatseni ine kuno m'mbale mutu wa Yohane Mbatizi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo iye, atampangira amake, anati, Ndipatseni ine kuno m'mbale mutu wa Yohane Mbatizi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono mai wake atamuuza choti apemphe, mwana wamkazi uja adati, “Mundipatse pompano mutu wa Yohane Mbatizi m'mbale.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo atamupangira amayi ake anati, “Mundipatse pomwe pano mutu wa Yohane Mʼbatizi mʼmbale.” Onani mutuwo |