Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:7 - Buku Lopatulika

7 Pomwepo iye anamlonjeza chilumbirire, kumpatsa iye chimene chilichonse akapempha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pomwepo iye anamlonjeza chilumbirire, kumpatsa iye chimene chilichonse akapempha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Motero Herode adaalonjeza molumbira kuti, “Ndithudi, ndidzakupatsa chilichonse chimene ungapemphe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Kotero Herode analonjeza ndi lumbiro kumupatsa chilichonse chimene mwanayo angamupemphe.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:7
6 Mawu Ofanana  

Ninena naye mfumu, Mufunanji, Estere mkazi wamkulu? Pempho lanu nchiyani? Lidzaperekedwa kwa inu, kufikira limodzi la magawo awiri a ufumuwo.


Ndipo mfumu inati kwa Estere pa madyerero a vinyo, Pempho lanu nchiyani? Lidzaperekedwa kwa inu; mufunanji? Chidzachitika, kufikira limodzi la magawo awiri a ufumuwo.


Nitinso mfumu kwa Estere tsiku lachiwirili pa madyerero a vinyo, Pempho lanu nchiyani, mkazi wamkulu Estere? Lidzapatsidwa kwa inu; mufunanji? Chidzachitika, kufikira limodzi la magawo awiri a ufumu wanga.


Wotsinzina ndiye aganizira zokhota; wosunama afikitsa zoipa.


Koma pakufika tsiku la kubadwa kwake kwa Herode, mwana wamkazi wa Herodiasi anavina pakati pao, namkondweretsa Herode.


Ndipo iye, atampangira amake, anati, Ndipatseni ine kuno m'mbale mutu wa Yohane Mbatizi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa