Mateyu 14:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo pofuna kumupha iye, anaopa khamu la anthu, popeza anamuyesa iye mneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo pofuna kumupha iye, anaopa khamu la anthu, popeza anamuyesa iye mneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kwenikweni Herode ankafuna kupha Yohane, koma ankaopa anthu, chifukwa iwo ankati ndi mneneri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Herode anafuna kupha Yohane koma iye anaopa anthu chifukwa anamuyesa iye mneneri. Onani mutuwo |