Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo pofuna kumupha iye, anaopa khamu la anthu, popeza anamuyesa iye mneneri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo pofuna kumupha iye, anaopa khamu la anthu, popeza anamuyesa iye mneneri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Kwenikweni Herode ankafuna kupha Yohane, koma ankaopa anthu, chifukwa iwo ankati ndi mneneri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Herode anafuna kupha Yohane koma iye anaopa anthu chifukwa anamuyesa iye mneneri.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:5
10 Mawu Ofanana  

ndipo pamene Yehoyakimu mfumu, ndi amphamvu ake onse, ndi akulu onse, anamva mau ake, mfumu inafuna kumupha iye; koma pamene Uriya anamva, anaopa, nathawa, nanka ku Ejipito;


Koma munatulukiranji? Kukaona mneneri kodi? Indetu, ndinena kwa inu, wakuposa mneneri.


Koma tikati, Kwa anthu, tiopa khamulo la anthu; pakuti onse amuyesa Yohane mneneri.


Popeza Yohane anadza kwa inu m'njira ya chilungamo, ndipo simunamvere iye; koma amisonkho ndi akazi achiwerewere anammvera iye; ndipo inu, m'mene munachiona, simunalape pambuyo pake, kuti mumvere iye.


Ndiponso, tikanena, Uchokera kwa anthu; anthu onse adzatiponya miyala: pakuti akopeka mtima, kuti Yohane ali mneneri.


Koma m'mene anawaopsanso anawamasula, osapeza kanthu kakuwalanga, chifukwa cha anthu; pakuti onse analemekeza Mulungu chifukwa cha chomwe chidachitika.


Pamenepo anachoka mdindo pamodzi ndi anyamata; anadza nao, koma osawagwiritsa, pakuti anaopa anthu, angaponyedwe miyala.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa