Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:7 - Buku Lopatulika

7 Koma zina zinagwa paminga, ndipo mingayo inayanga, nkuzitsamwitsa izo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Koma zina zinagwa paminga, ndipo mingayo inayanga, nizitsamwitsa izo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Mbeu zina zidagwera pa zitsamba zaminga. Zitsambazo pokula zidalanda chakudya cha mbeu zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Mbewu zina zinagwa pa minga ndipo mingayo inayanga ndi kuzirepheretsa kukula.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:7
8 Mawu Ofanana  

minga ndi mitula idzakubalira iwe; ndipo udzadya therere la m'thengo:


Ndipo iye amene afesedwa kuminga, uyu ndiye wakumva mau; ndipo kulabadira kwa dziko lapansi, ndi chinyengo cha chuma chitsamwitsa mau, ndipo akhala wopanda chipatso.


Ndipo m'mene dzuwa linakwera zinapserera; ndipo popeza zinalibe mizu zinafota.


Koma zina zinagwa pa nthaka yabwino, ndipo zinabala zipatso, zina za makumi khumi, zina za makumi asanu ndi limodzi, zina za makumi atatu.


Ndipo zina zinagwa paminga, ndipo minga inakula, nkuzitsamwitsa, ndipo sizinabale zipatso.


Ndipo zina zinagwa pakati pa minga; ndi mingayo inaphuka pamodzi nazo, nkuzitsamwitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa