Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:53 - Buku Lopatulika

53 Ndipo panali, pamene Yesu anatha mafanizo awa, anachokera kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

53 Ndipo panali, pamene Yesu anatha mafanizo awa, anachokera kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

53 Yesu atatsiriza kunena mafanizoŵa, adachoka kumeneko.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

53 Yesu atatsiriza mafanizowa anachoka kumeneko.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:53
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Chifukwa chake, mlembi aliyense, wophunzitsidwa mu Ufumu wa Kumwamba, ali wofanana ndi munthu mwini banja, amene atulutsa m'chuma chake zinthu zakale ndi zatsopano.


Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa