Mateyu 13:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo monga namsongole asonkhanitsidwa pamodzi, natenthedwa pamoto, motero mudzakhala m'chimaliziro cha nthawi ya pansi pano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo monga namsongole asonkhanitsidwa pamodzi, natenthedwa pamoto, motero mudzakhala m'chimaliziro cha nthawi ya pansi pano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Monga momwe adaazulira namsongole uja nkumutentha pa moto, zidzateronso pa kutha kwa dziko lino lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 “Monga momwe namsongole azulidwa ndi kutenthedwa ndi moto, momwemonso kudzakhala pakutha kwa dziko. Onani mutuwo |