Mateyu 13:29 - Buku Lopatulika29 Koma iye anati, Iai, kuti kapena m'mene mukasonkhanitsa namsongoleyo, mungazulenso tirigu pamodzi naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Koma iye anati, Iai, kuti kapena m'mene mukasonkhanitsa namsongoleyo, mungazulenso tirigu pamodzi naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Koma iye adati, ‘Iyai, mungakazulire kumodzi ndi tirigu pozula namsongoleyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 “Iye anakana nati, ‘Ayi. Chifukwa pamene mukuzula namsongoleyo mwina inu mungazulire pamodzi ndi tirigu. Onani mutuwo |