Mateyu 13:15 - Buku Lopatulika15 Chifukwa unalemera mtima wa anthu awa, ndipo m'makutu ao anamva mogontha, ndipo maso ao anatsinzina; kuti asaone konse ndi maso, asamve ndi makutu, asazindikire ndi mtima wao, asatembenuke, ndipo ndisawachiritse iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Chifukwa unalemera mtima wa anthu awa, ndipo m'makutu ao anamva mogontha, ndipo maso ao anatsinzina; kuti asaone konse ndi maso, asamve ndi makutu, asazindikire ndi mtima wao, asatembenuke, ndipo ndisawachiritse iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndithu anthu ameneŵa nzeru zao nzobuntha, adagonthetsa makutu ao, ndipo adapsinya maso ao, kuwopa kuti angamapenye ndi maso aowo, angamamve ndi makutu aowo, angamamvetse ndi nzeru zaozo, ndi kutembenuka mtima, Ineyo nkuŵachiritsa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Pakuti mtima wa anthu awa ndi wokanika, mʼmakutu mwawo ndi mogontha, ndipo atsinzina kuti asaone kanthu. Mwina angapenye ndi maso awo, angamve ndi makutu awo, angamvetse ndi nzeru zawo ndi kutembenuka, Ineyo nʼkuwachiritsa.’ Onani mutuwo |