Mateyu 12:30 - Buku Lopatulika30 Iye wosakhala pamodzi ndi Ine akana Ine, ndi iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwazamwaza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Iye wosakhala pamodzi ndi Ine akana Ine, ndi iye wosasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amwazamwaza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 “Munthu wosavomerezana ndi Ine, ndiye kuti ndi wotsutsana nane. Ndipo wosandithandiza kusonkhanitsa, ndiye kuti ameneyo ndi womwaza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Iye amene sali ndi Ine atsutsana nane ndipo iye amene sasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amamwaza. Onani mutuwo |