Mateyu 12:24 - Buku Lopatulika24 Koma Afarisi pakumva, anati, Uyu samatulutsa ziwanda koma ndi mphamvu yake ya Belezebulu, mkulu wa ziwanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma Afarisi pakumva, anati, Uyu samatulutsa ziwanda koma ndi mphamvu yake ya Belezebulu, mkulu wa ziwanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma Afarisi atamva zimenezi adati, “Iyai, mphamvu zimene iyeyu amatulutsira mizimu yoipa sizichokeratu kwina, koma kwa Belezebulu, mkulu wa mizimu yoipayo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Afarisi atamva zimenezi, anati, “Uyu amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu mkulu wa ziwandazo.” Onani mutuwo |