Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 12:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo makamu onse a anthu anazizwa, nanena, Uyu si mwana wa Davide kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo makamu onse a anthu anazizwa, nanena, Uyu si mwana wa Davide kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Anthu onse adazizwa kwambiri nkumanena kuti, “Kodi ameneyu sangakhale Mwana uja wa Davide?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Anthu onse anadabwa ndipo anati, “Kodi uyu ndi kukhala mwana wa Davide?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 12:23
9 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, mkazi wa ku Kanani anatuluka m'malire, nafuula, nati, Mundichitire ine chifundo Ambuye, mwana wa Davide; mwana wanga wamkazi wagwidwa koopsa ndi chiwanda.


Ndipo mipingo yakumtsogolera ndi yakumtsatira, inafuula, kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide! Wolemekezeka ndiye wakudza m'dzina la Ambuye! Hosana mu Kumwambamwamba!


Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake:


Ndipo popita Yesu kuchokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, ofuula ndi kuti, Mutichitire ife chifundo, mwana wa Davide.


Ndipo m'mene chinatulutsidwa chiwandacho, wosalankhulayo analankhula, ndipo makamu a anthu anazizwa, nanena, Kale lonse sichinaoneke chomwecho mwa Israele.


Tiyeni, mukaone munthu, amene anandiuza zinthu zilizonse ndinazichita: ameneyu sali Khristu nanga?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa