Mateyu 12:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo makamu onse a anthu anazizwa, nanena, Uyu si mwana wa Davide kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo makamu onse a anthu anazizwa, nanena, Uyu si mwana wa Davide kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Anthu onse adazizwa kwambiri nkumanena kuti, “Kodi ameneyu sangakhale Mwana uja wa Davide?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Anthu onse anadabwa ndipo anati, “Kodi uyu ndi kukhala mwana wa Davide?” Onani mutuwo |