Mateyu 12:20 - Buku Lopatulika20 bango lophwanyika sadzalithyola, ndi nyali yofuka sadzaizima, kufikira Iye adzatumiza chiweruzo chikagonjetse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 bango lophwanyika sadzalithyola, ndi nyali yofuka sadzaizima, kufikira Iye adzatumiza chiweruzo chikagonjetse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Iye sadzatsiriza bango lothyoka, nyale yofuka sadzaizimitsa, mpaka atapambanitsa chilungamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Bango lophwanyika sadzalithyola, ndi nyale yofuka sadzayizimitsa, kufikira Iye adzatumiza chiweruziro chikagonjetse. Onani mutuwo |