Mateyu 12:19 - Buku Lopatulika19 Sadzalimbana, sadzafuula; ngakhale mmodzi sadzamva mau ake m'makwalala; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Sadzalimbana, sadzafuula; ngakhale mmodzi sadzamva mau ake m'makwalala; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iye sadzachita makani, kapena kufuula. Palibe munthu wodzamva mau ake m'miseu ya m'mizinda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Sadzalimbana, sadzafuwula, ngakhale mmodzi sadzamva mawu ake mʼmakwalala. Onani mutuwo |