Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 10:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo iye amene satenga mtanda wake, natsata pambuyo panga, sayenera Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo iye amene satenga mtanda wake, natsata pambuyo panga, sayenera Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Amene sasenza mtanda wake ndi kumanditsata, ngwosayenera kukhala wophunzira wanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Aliyense amene satenga mtanda wake ndi kunditsata Ine sayenera kukhala wanga.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 10:38
7 Mawu Ofanana  

Pomwepo Yesu anati kwa ophunzira ake, Ngati munthu afuna kudza pambuyo panga, adzikane yekha, natenge mtanda wake, nanditsate Ine.


Ndipo pakutuluka pao anapeza munthu wa ku Kirene, dzina lake Simoni, namkakamiza iye kuti anyamule mtanda wake.


Ndipo Yesu anamyang'ana, namkonda, nati kwa iye, Chinthu chimodzi chikusowa: pita, gulitsa zonse uli nazo, nuzipereke kwa anthu aumphawi, ndipo chuma udzakhala nacho m'mwamba; ndipo ukadze kuno, unditsate Ine.


Ndipo anadziitanira khamulo la anthu pamodzi ndi ophunzira ake, nati kwa iwo, Ngati munthu afuna kudza pambuyo panga, adzikanize yekha, nanyamule mtanda wake, nanditsate Ine.


Ndipo aliyense amene sasenza mtanda wake wa mwini yekha, ndi kudza pambuyo panga, sangathe kukhala wophunzira wanga.


ndipo anasenza mtanda yekha, natuluka kunka kumalo otchedwa Malo a Bade, amene atchedwa mu Chihebri, Gologota:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa