Mateyu 10:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo iye amene satenga mtanda wake, natsata pambuyo panga, sayenera Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo iye amene satenga mtanda wake, natsata pambuyo panga, sayenera Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Amene sasenza mtanda wake ndi kumanditsata, ngwosayenera kukhala wophunzira wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Aliyense amene satenga mtanda wake ndi kunditsata Ine sayenera kukhala wanga. Onani mutuwo |