Mateyu 10:17 - Buku Lopatulika17 Koma chenjerani ndi anthu; pakuti adzakuperekani inu ku bwalo la akulu a milandu, nadzakukwapulani inu m'masunagoge mwao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma chenjerani ndi anthu; pakuti adzakuperekani inu kwa akulu a mlandu, nadzakukwapulani inu m'masunagoge mwao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Anthu muchenjere nawo, pakuti adzakuperekani ku mabwalo amilandu, ndipo adzakukwapulani m'nyumba zao zamapemphero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Chenjerani ndi anthu pakuti adzakuperekani ku mabwalo amilandu nadzakukwapulani mʼmasunagoge mwawo. Onani mutuwo |