Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 10:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo ngati nyumbayo ili yoyenera, mtendere wanu udze pa iyo, koma ngati siili yoyenera, mtendere wanu ubwerere kwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo ngati nyumbayo ili yoyenera, mtendere wanu udze pa iyo, koma ngati siili yoyenera, mtendere wanu ubwerere kwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Tsono ngati anthu am'nyumbamo akulandiranidi, mtendere wanuwo ukhale nawo ndithu. Koma ngati anthu am'nyumbamo akana kukulandirani, mtendere wanuwo ubwerere kwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Mtendere wanu ukhale pa a mʼnyumbayo ngati ndi oyenera. Koma ngati siwoyenera, mtendere wanu ubwerere kwa inu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 10:13
5 Mawu Ofanana  

Koma ine, pakudwala iwowa, chovala changa ndi chiguduli. Ndinazunza moyo wanga ndi kusala; ndipo pemphero langa linabwera kuchifuwa changa.


Ndipo polowa m'nyumba muwalonjere.


Ndipo yemwe sadzakulandirani inu kapena kusamva mau anu, pamene mulikutuluka m'nyumbayo, kapena m'mudzimo, sansani fumbi m'mapazi anu.


Ndipo mukakhala mwana wa mtendere m'menemo, mtendere wanu udzapumula pa iye; koma ngati mulibe, udzabwerera kwa inu.


koma kwa ena fungo la moyo kumoyo. Ndipo azikwanira ndani izi?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa