Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 1:13 - Buku Lopatulika

13 ndi Zerubabele anabala Abihudi; ndi Abihudi anabala Eliyakimu; ndi Eliyakimu anabala Azoro;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 ndi Zerubabele anabala Abihudi; ndi Abihudi anabala Eliyakimu; ndi Eliyakimu anabala Azoro;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Zerubabele adabereka Abihudi, Abihudi adabereka Eliyakimu, Eliyakimu adabereka Azoro.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Zerubabeli anabereka Abiudi, Abiudi anabereka Eliakimu, Eliakimu anabereka Azoro.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 1:13
3 Mawu Ofanana  

Chaka chachiwiri cha mfumu Dariusi, mwezi wachisanu ndi chimodzi, mau a Yehova anadza mwa Hagai mneneri kwa Zerubabele mwana wa Sealatiele, chiwanga cha Yuda, ndi kwa Yoswa mwana wa Yehozadaki, mkulu wa ansembe, ndi kuti,


Ndipo pambuyo pake pa kutengedwako ku Babiloni, Yekoniya anabala Sealatiele; ndi Sealatiele anabala Zerubabele;


ndi Azoro anabala Zadoki; ndi Zadoki anabala Akimu; ndi Akimu anabala Eliudi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa