Masalimo 94:16 - Buku Lopatulika16 Adzandiukira ndani kutsutsana nao ochita zoipa? Adzandilimbikira ndani kutsutsana nao ochita zopanda pake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Adzandiukira ndani kutsutsana nao ochita zoipa? Adzandilimbikira ndani kutsutsana nao ochita zopanda pake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndani amalimba mtima kuti andimenyere nkhondo ndi anthu oipa? Ndani amaimira mbali yanga, kuti alimbane ndi anthu ochita zoipa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndani adzadzuka chifukwa cha ine kulimbana ndi anthu oyipa? Ndani adzayimirira mʼmalo mwanga kulimbana ndi anthu ochita zoyipa? Onani mutuwo |