Masalimo 94:17 - Buku Lopatulika17 Akadapanda kukhala thandizo langa Yehova, moyo wanga ukadakhala kuli chete. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Akadapanda kukhala thandizo langa Yehova, moyo wanga ukadakhala kuli chete. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Chauta akadapanda kundithandiza, bwenzi posachedwa nditapita ku dziko lazii. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Yehova akanapanda kundithandiza, bwenzi nditakakhala msanga ku malo achete a imfa. Onani mutuwo |