Masalimo 91:4 - Buku Lopatulika4 Adzakufungatira ndi nthenga zake, ndipo udzathawira kunsi kwa mapiko ake; choonadi chake ndicho chikopa chotchinjiriza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Adzakufungatira ndi nthenga zake, ndipo udzathawira kunsi kwa mapiko ake; choonadi chake ndicho chikopa chotchinjiriza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adzakuphimba ndi nthenga za mapiko ake, udzapeza malo othaŵirako m'mapikomo. Kukhulupirika kwake kumateteza monga chishango ndi lihawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Adzakuphimba ndi nthenga zake, ndipo udzapeza malo othawira mʼmapikomo; kukhulupirika kwake kudzakhala chishango chako ndi lihawo. Onani mutuwo |