Masalimo 91:2 - Buku Lopatulika2 Ndidzati kwa Yehova, Pothawirapo panga ndi linga langa; Mulungu wanga, amene ndimkhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidzati kwa Yehova, Pothawirapo panga ndi linga langa; Mulungu wanga, amene ndimkhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 adzanena kwa Chauta kuti, “Inu ndinu kothaŵira kwanga ndi linga langa, ndinu Mulungu wanga amene ndimakukhulupirirani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzanena za Yehova, “Iye ndiye pothawira panga ndi linga langa, Mulungu wanga amene ndimadalira.” Onani mutuwo |