Masalimo 91:1 - Buku Lopatulika1 Iye amene akhala pansi m'ngaka yake ya Wam'mwambamwamba adzagonera mu mthunzi wa Wamphamvuyonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Iye amene akhala pansi m'ngaka yake ya Wam'mwambamwamba adzagonera mu mthunzi wa Wamphamvuyonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Munthu amene amakhala m'linga la Wopambanazonse, iye amene amakhala mumthunzi mwa Mphambe, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Iye amene amakhala mu mthunzi wa Wammwambamwamba adzapuma mu mthunzi wa Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |