Masalimo 9:10 - Buku Lopatulika10 ndipo iwo akudziwa dzina lanu adzakhulupirira Inu; pakuti, Inu Yehova, simunawasiye iwo akufuna Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo iwo akudziwa dzina lanu adzakhulupirira Inu; pakuti, Inu Yehova, simunawasiya iwo akufuna Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Amene amadziŵa dzina lanu, Inu Chauta, amakukhulupirirani, pakuti Inu Chauta simuŵasiya anthu okufunitsitsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iwo amene amadziwa dzina lanu adzadalira Inu, pakuti Inu Yehova, simunawatayepo amene amafunafuna inu. Onani mutuwo |