Masalimo 89:3 - Buku Lopatulika3 Ndinachita chipangano ndi wosankhika wanga, ndinalumbirira Davide mtumiki wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndinachita chipangano ndi wosankhika wanga, ndinalumbirira Davide mtumiki wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Inu mwanena kuti, “Ndachita chipangano ndi wosankhidwa wanga, ndalumbira kwa Davide mtumiki wanga kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Inu munati, “Ndachita pangano ndi wosankhidwa wanga, ndalumbira kwa Davide mtumiki wanga kuti, Onani mutuwo |