Masalimo 89:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti ndinati, Chifundo adzachimanga kosaleka; mudzakhazika chikhulupiriko chanu mu Mwamba mwenimweni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti ndinati, Chifundo adzachimanga kosaleka; mudzakhazika chikhulupiriko chanu m'Mwamba mwenimweni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chikondi chanu chosasinthika chakhazikika kuti chikhale mpaka muyaya, kukhulupirika kwanu nkwachikhalire ngati mlengalenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzalalikira kuti chikondi chanu chidzakhazikika mpaka muyaya, kuti Inu munakhazikitsa kukhulupirika kwanu kumwamba kwenikweniko. Onani mutuwo |