Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 86:7 - Buku Lopatulika

7 Tsiku la msauko wanga ndidzaitana Inu; popeza mudzandivomereza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Tsiku la msauko wanga ndidzaitana Inu; popeza mudzandivomereza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Pa tsiku lamavuto ndimakuitanani, pakuti mumayankha mapemphero anga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Pa tsiku la mavuto anga ndidzayitana Inu, pakuti Inu mudzandiyankha.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 86:7
14 Mawu Ofanana  

Ndifuula nalo liu langa kwa Yehova; ndi mau anga ndipemba kwa Yehova.


Pamene mzimu wanga unakomoka m'kati mwanga, munadziwa njira yanga. M'njira ndiyendamo ananditchera msampha.


Ine ndinakuitanani, pakuti mudzandiyankha, Mulungu; tcherani khutu lanu kwa ine, imvani mau anga.


M'kusauka kwanga ndinaitana Yehova, ndipo ndinakuwira Mulungu wanga; mau anga anawamva mu Kachisi mwake, ndipo mkuwo wanga wa pankhope pake unalowa m'makutu mwake.


Ndipo undiitane tsiku la chisautso, ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza.


Adzandifuulira Ine ndipo ndidzamyankha; kunsautso ndidzakhala naye pamodzi; ndidzamlanditsa, ndi kumchitira ulemu.


Yehova, iwo adza kwa Inu movutika, iwo anathira pemphero, muja munalikuwalanga.


Ndipo anati, Ndinaitana Yehova m'nsautso wanga, ndipo anandiyankha ine; ndinafuula ndili m'mimba ya manda, ndipo munamva mau anga.


Ndipo pokhala Iye m'chipsinjo mtima anapemphera kolimba koposa ndithu: ndi thukuta lake linakhala ngati madontho aakulu a mwazi alinkugwa pansi.


Ameneyo, m'masiku a thupi lake anapereka mapemphero ndi mapembedzero pamodzi ndi kulira kwakukulu ndi misozi kwa Iye amene anakhoza kumpulumutsa Iye muimfa, ndipo anamveka popeza anaopa Mulungu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa