Masalimo 86:7 - Buku Lopatulika7 Tsiku la msauko wanga ndidzaitana Inu; popeza mudzandivomereza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tsiku la msauko wanga ndidzaitana Inu; popeza mudzandivomereza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pa tsiku lamavuto ndimakuitanani, pakuti mumayankha mapemphero anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pa tsiku la mavuto anga ndidzayitana Inu, pakuti Inu mudzandiyankha. Onani mutuwo |