Masalimo 86:16 - Buku Lopatulika16 Mundibwerere ine, ndi kundichitira chifundo; mpatseni mtumiki wanu mphamvu yanu, ndipo pulumutsani mwana wa mdzakazi wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Mundibwerere ine, ndi kundichitira chifundo; mpatseni mtumiki wanu mphamvu yanu, ndipo pulumutsani mwana wa mdzakazi wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mundiyang'ane ndipo mundichitire chifundo. Mundipatse mphamvu zanu ine mtumiki wanu, mundipulumutse ine mwana wa mdzakazi wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Tembenukirani kwa ine ndipo ndichitireni chifundo; perekani mphamvu zanu kwa mtumiki wanu ndipo pulumutsani mwana wa mdzakazi wanu. Onani mutuwo |