Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 86:17 - Buku Lopatulika

17 Mundichitire chizindikiro choti chabwino; kuti ondida achione, nachite manyazi, popeza Inu, Yehova, munandithandiza ndi kundisangalatsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Mundichitire chizindikiro choti chabwino; kuti ondida achione, nachite manyazi, popeza Inu, Yehova, munandithandiza ndi kundisangalatsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Mundiwonetse chizindikiro chakuti mumandikomera mtima, kuti odana nane achite manyazi. Adzaona kuti Inu Chauta mwandithandiza ndi kundilimbitsa mtima.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Mundionetse chizindikiro cha ubwino wanu kuti adani achione ndi kuchititsidwa manyazi, pakuti Yehova mwandithandiza ndi kunditonthoza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 86:17
11 Mawu Ofanana  

Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda.


Kuyembekeza ndayembekeza Yehova; ndipo anandilola, namva kufuula kwanga.


Sitiziona zizindikiro zathu; palibenso mneneri; ndipo mwa ife palibe wina wakudziwa mpaka liti.


Tsiku lomwelo udzati, Ndikuyamikani inu Yehova; pakuti ngakhale munandikwiyira, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mutonthoza mtima wanga.


Hezekiya anatinso, Chizindikiro nchiyani, kuti ndidzakwera kunka kunyumba ya Yehova?


kumpereka iye wochita chotere kwa Satana, kuti lionongeke thupi, kuti mzimu upulumutsidwe m'tsiku la Ambuye Yesu.


Ndipo anati kwa Iye, Ngati mundikomera mtima mundionetse chizindikiro tsopano chakuti ndi Inu wakunena nane.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa