Masalimo 85:9 - Buku Lopatulika9 Indedi chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo akumuopa Iye; kuti m'dziko mwathu mukhale ulemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Indedi chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo akumuopa Iye; kuti m'dziko mwathu mukhale ulemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Zoonadi, Mulungu ali wokonzekera kuti apulumutse amene amamuwopa, kuti ulemerero wake ukhale m'dziko lathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndithu chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo amene amaopa Iye, kuti ulemerero wake ukhale mʼdziko lathu. Onani mutuwo |