Masalimo 85:11 - Buku Lopatulika11 Choonadi chiphukira m'dziko; ndi chilungamo chasuzumira chili m'mwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Choonadi chiphukira m'dziko; ndi chilungamo chasuzumira chili m'mwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu ake adzakhala okhulupirika pansi pano, ndipo Mulungu wakumwamba adzaŵalungamitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kukhulupirika kumatumphuka kuchokera ku dziko lapansi, ndipo chilungamo chimayangʼana pansi kuchokera kumwamba. Onani mutuwo |