Masalimo 79:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anansi athu amene anatonza Inu muwabwezere chotonza chao, kasanu ndi kawiri kumtima kwao, Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anansi athu amene anatonza Inu muwabwezere chotonza chao, kasanu ndi kawiri kumtima kwao, Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu Ambuye, kunyoza kuja kumene anthu a mitundu ina adakunyozani, muŵabwezere kasanunkaŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Mubwezere kwa anansi athu kasanu nʼkawiri kunyoza kumene ananyoza Inu Ambuye. Onani mutuwo |