Masalimo 79:11 - Buku Lopatulika11 Kubuula kwa wandende kufike kuli Inu; monga mwa mphamvu yanu yaikulu lolani ana a imfa atsale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kubuula kwa wandende kufike kuli Inu; monga mwa mphamvu yanu yaikulu lolani ana a imfa atsale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mumve kubuula kwa anthu am'ndende, muŵasunge ndi mphamvu zanu zazikulu anthu oyenera kuphedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kubuwula kwa anthu a mʼndende kufike pamaso panu; ndi mphamvu ya dzanja lanu muwasunge amene aweruzidwa kuti aphedwe. Onani mutuwo |