Masalimo 78:7 - Buku Lopatulika7 Ndi kuti chiyembekezo chao chikhale kwa Mulungu, osaiwala zochita Mulungu, koma kusunga malamulo ake ndiko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi kuti chiyembekezo chao chikhale kwa Mulungu, osaiwala zochita Mulungu, koma kusunga malamulo ake ndiko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anawo aike chikhulupiriro chao pa Mulungu, ndipo asaiŵale ntchito za Mulungu, koma asunge malamulo ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho iwo adzakhulupirira Mulungu ndipo sadzayiwala ntchito zake koma adzasunga malamulo ake. Onani mutuwo |