Masalimo 78:16 - Buku Lopatulika16 Anatulukitsa mitsinje m'thanthwe, inde anatsikitsa madzi ngati mitsinje. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Anatulukitsa mitsinje m'thanthwe, inde anatsikitsa madzi ngati mitsinje. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Adatumphutsa mifuleni m'thanthwe, nayendetsa madzi ngati mitsinje. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Anatulutsa mitsinje kuchokera mʼmingʼalu ya miyala ndi kuyenda madzi ngati mitsinje. Onani mutuwo |