Masalimo 78:15 - Buku Lopatulika15 Anang'alula thanthwe m'chipululu, ndipo anawamwetsa kochuluka monga m'madzi ozama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Anang'alula thanthwe m'chipululu, ndipo anawamwetsa kochuluka monga m'madzi ozama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Adang'amba matanthwe am'chipululu, naŵapatsa madzi ochuluka ngati amumtsinje, kuti amwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iye anangʼamba miyala mʼchipululu ndi kuwapatsa madzi ochuluka ngati a mʼnyanja zambiri; Onani mutuwo |