Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 78:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo anaiwala zochita Iye, ndi zodabwitsa zake zimene anawaonetsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo anaiwala zochita Iye, ndi zodabwitsa zake zimene anawaonetsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Iwo adaiŵala zimene Mulungu adachita, ndiponso zozizwitsa zimene Iye adaŵaonetsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Anayiwala zimene Iye anachita, zozizwitsa zimene anawaonetsa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 78:11
5 Mawu Ofanana  

Koma anaiwala ntchito zake msanga; sanalindire uphungu wake:


Ndi kuti chiyembekezo chao chikhale kwa Mulungu, osaiwala zochita Mulungu, koma kusunga malamulo ake ndiko.


Kodi angathe namwali kuiwala zokometsera zake, kapena mkwatibwi zovala zake? Koma anthu anga andiiwala Ine masiku osawerengeka.


Mwaleka Thanthwe limene linakubalani, mwaiwala Mulungu amene anakulengani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa