Masalimo 74:1 - Buku Lopatulika1 Mulungu, munatitayiranji chitayire? Mkwiyo wanu ufukiranji pa nkhosa za kubusa kwanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mulungu, munatitayiranji chitayire? Mkwiyo wanu ufukiranji pa nkhosa za kubusa kwanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Mulungu, chifukwa chiyani mukutitaya mpaka muyaya? Chifukwa chiyani mkwiyo wanu ukutukutirira nkhosa za busa lanu ngati moto? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nʼchifukwa chiyani mwatitaya ife kwamuyaya, Inu Mulungu? Chifukwa chiyani mkwiyo wanu ukutukutira pa nkhosa za busa lanu? Onani mutuwo |