Masalimo 73:25 - Buku Lopatulika25 Ndili ndi yani Kumwamba, koma Inu? Ndipo padziko lapansi palibe wina wondikonda koma Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndili ndi yani Kumwamba, koma Inu? Ndipo pa dziko lapansi palibe wina wondikonda koma Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Nanga ndili ndi yani kumwamba kupatula Inu? Pansi pano palibe kanthu kena kamene ndimafuna, koma Inu nokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Kodi kumwamba ndili ndi yani kupatula Inu? Ndipo dziko lapansi lilibe chilichonse chimene ndimachilakalaka koposa Inuyo. Onani mutuwo |